Mawu a M'munsi
b Hamani ayenera kuti anali m’gulu la Aamaleki ochepa kwambiri omwe analipobe pa nthawiyi, chifukwa anthu “otsala” a mtundu umenewu anali ataphedwa kale m’nthawi ya Mfumu Hezekiya.—1 Mbiri 4:43.
b Hamani ayenera kuti anali m’gulu la Aamaleki ochepa kwambiri omwe analipobe pa nthawiyi, chifukwa anthu “otsala” a mtundu umenewu anali ataphedwa kale m’nthawi ya Mfumu Hezekiya.—1 Mbiri 4:43.