Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mawu amene amagwiritsa ntchito ponena za mabuku owonjezera a m’Baibulo (apocryphal) anachokera ku mawu achigiriki amene amatanthauza “kubisa.” Poyamba mawu amenewa ankanena za nkhani zimene zinkaphunzitsidwa pasukulu ina koma ankazibisa kuti amene saphunzira pasukulupo asazidziwe. Koma m’kupita kwa nthawi, mawuwa anayambanso kugwiritsidwa ntchito ponena za mabuku omwe sanaphatikizidwe m’gulu la mabuku ovomerezeka a m’Baibulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena