Mawu a M'munsi
a Baibulo limatchula kangapo konse kuti Saulo ankazunzanso akazi. Zimenezi zimasonyeza kuti akazi ankachita zambiri pa ntchito yolalikira monga mmene amachitiranso masiku ano.—Sal. 68:11.
a Baibulo limatchula kangapo konse kuti Saulo ankazunzanso akazi. Zimenezi zimasonyeza kuti akazi ankachita zambiri pa ntchito yolalikira monga mmene amachitiranso masiku ano.—Sal. 68:11.