Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

e Ndime 13: Mawu a mtumwi Paulo pa lemba la Machitidwe 20:29, 30 anasonyeza kuti mpingo udzasokonezedwa ndi anthu ochokera mbali ziwiri. Poyamba, ananena kuti Akhristu onyenga (“namsongole”) ‘adzafika pakati pa’ Akhristu oona. Kenako ananena kuti ‘pakati pa’ Akhristu oonawo, ena adzapatuka n’kuyamba kulankhula “zinthu zopotoka.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena