Mawu a M'munsi
a N’zoona kuti anthu ayenera kuyesetsa kukhululukirana ndiponso kulimbana ndi mavuto a m’banja lawo. Koma ngati wina wachita chigololo, Baibulo limalola wolakwiridwayo kusankha zochita. Akhoza kukhululuka kapena kuthetsa banjalo. (Mat 19:9) Onani nkhani yakuti “Lingaliro la Baibulo: Chigololo—Kukhululukira Kapena Kusakhululukira?” mu Galamukani ya August 8, 1995.