Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Matendawa alipo a mitundu ingapo ndipo amakhudza mbali ya ubongo imene imathandiza kuti manja ndi miyendo zizigwira ntchito. Matendawa amapangitsanso kuti munthu azidwala matenda akugwa, azivutika kudya komanso azilephera kulankhula. Mtundu wa matenda amene Jairo amadwala ndi woopsa kwambiri ndipo umachititsa kuti manja ndi miyendo ziume komanso kuti khosi lake likhale lawedewede.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena