Mawu a M'munsi
a Nkhaniyi ndiponso yotsatira kwenikweni alembera akulu koma aliyense mumpingo ayenera kuganizira bwino mfundo zake. Tikutero chifukwa chakuti nkhanizi zilimbikitsa m’bale aliyense wobatizidwa kuti aphunzitsidwe n’cholinga choti athandize pa ntchito za mumpingo. Zikatero, aliyense mumpingo adzapindula kwambiri.