Mawu a M'munsi
a Ngati wachinyamata akukonda kwambiri Yehova, ndi wodzichepetsa ndipo akukwaniritsa zimene Malemba amanena, akulu angamuvomereze kukhala mtumiki wothandiza ngakhale kuti sanakwanitse zaka 20.—1 Tim. 3:8-10, 12; onani Nsanja ya Olonda ya July 1, 1989, tsamba 29.