Mawu a M'munsi
a Anthu ena sakhulupirira Baibulo chifukwa cha zimene matchalitchi ena amaphunzitsa. Matchalitchiwa amaphunzitsa kuti dziko lapansili ndiye pakati pa chilengedwe chonse komanso kuti Mulungu analenga dzikoli m’masiku 6 enieni a maola 24.—Onani bokosi lakuti, “Baibulo Silitsutsana Ndi Mfundo Zolondola Zasayansi.”