Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nyimbo ya Debora imasonyeza kuti nthawi zambiri Sisera akamachoka kunkhondo, ankabwerako ndi zinthu zosiyanasiyana komanso atsikana moti nthawi zina msilikali aliyense ankapatsidwa atsikana angapo. (Oweruza 5:30) Zikuoneka kuti atsikanawa ankawatenga kuti azigonana nawo basi ndipo pa nthawiyi ku Kanani azimayi ambiri ankagwiriridwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena