Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Aisiraeli sanalengeze mfundo za mtendere asanakamenyane ndi Akanani chifukwa choti Akananiwo anali okanika. Anali atapatsidwa nthawi yokwanira yoti asinthe makhalidwe awo oipa. Koma ayi ndithu sanasinthe, moti pa nthawi imene Aisiraeli ankabwera kuti amenyane nawo, makhalidwe awo anali ataipiratu. (Genesis 15:13-16) Choncho Aisiraeli ankafunika kuseseratu Akanani onse kupatulapo anthu amene anasintha makhalidwe awo.—Yoswa 6:25; 9:3-27.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena