Mawu a M'munsi
b Mulungu anasamutsa moyo wa Mwana wake kuchoka kumwamba n’kuuika m’mimba mwa Mariya. Zimenezi zinachititsa kuti Mariya akhale ndi pakati. Ndipo mzimu woyera unateteza Yesu kuti asatengere uchimo kwa Mariya.—Luka 1:31, 35.
b Mulungu anasamutsa moyo wa Mwana wake kuchoka kumwamba n’kuuika m’mimba mwa Mariya. Zimenezi zinachititsa kuti Mariya akhale ndi pakati. Ndipo mzimu woyera unateteza Yesu kuti asatengere uchimo kwa Mariya.—Luka 1:31, 35.