Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Akatswiri ena a Baibulo amanena kuti uthenga wa Inoki umene Yuda analemba anautenga m’buku lakuti Buku la Inoki. Koma Yuda sakanatenga uthengawu m’bukuli chifukwa nkhani zambiri za m’bukuli ndi zongopeka komanso si zoona kuti linalembedwa ndi Inoki ndipo silikudziwika kumene linachokera. N’zoona kuti bukuli lili ndi uthenga wa Inoki koma mwina olemba ake anautenga m’zolemba zina zakale kapena anachita kuuzidwa ndi anthu ena. N’kutheka kuti uthenga wa Inoki umene Yuda analembawu anautenganso kumene olemba Buku la Inoki anatenga uthengawu. Apo ayi, mwina anamva kwa Yesu, yemwe anali kumwamba pamene Inoki anali ndi moyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena