Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Anthu othawa kwawo akafika, akulu ayenera kutsatira mwamsanga malangizo opezeka pamutu 8, ndime 30 m’buku lakuti Gulu Lochita Chifuniro cha Yehova. Akulu angapemphe ofesi ya nthambi ya m’dziko lawo kuti iwathandize kuti azilumikizana ndi mipingo ya m’dziko lina. Akhoza kuchita zimenezi pogwiritsa ntchito webusaiti ya jw.org. Angachite bwinonso kufufuza mwanzeru kuti adziwe mpingo umene anthuwo akuchokera komanso moyo wawo wauzimu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena