Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

f Tiyeneranso kupewa magulu monga a achinyamata kapena a masewera amene amakhudzana ndi zipembedzo zonyenga. Mwachitsanzo, tiyenera kupewa kukhala m’mabungwe a achinyamata monga a YMCA (Young Men’s Christian Association) kapena YWCA (Young Women’s Christian Association) omwe amanena kuti zochita zawo si zachipembedzo kwenikweni. Koma zoona zake n’zakuti mabungwe amenewa anayambitsidwa ndi zipembedzo komanso amalimbikitsa mfundo zachipembedzo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena