Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Tikukhala m’dziko lomwe wolamulira wake ndi Satana yemwe ndi tate wake wa bodza. Choncho nthawi zambiri zimativuta kuti tiziyendabe m’choonadi. Nawonso Akhristu a munthawi ya atumwi ankakumana ndi vuto lomweli. Pofuna kuwathandiza komanso kutithandiza ifeyo, Yehova anauzira mtumwi Yohane kulemba makalata atatu. Mfundo za m’makalatawa zitithandiza kudziwa zinthu zimene zingachititse kuti tisiye kuyenda m’choonadi komanso zomwe tingachite kuti tisagonje.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena