Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mwamuna akakwatira, amakhala mutu wa banja lake. Munkhaniyi tikambirana zimene kukhala mutu kumatanthauza, chifukwa chake Yehova anakonza zoti ena azikhala ndi udindo wotsogolera komanso zimene amuna angaphunzire kwa Yehova ndi Yesu. Munkhani yotsatira, tidzaona zimene amuna ndi akazi angaphunzire kwa Yesu komanso anthu ena otchulidwa m’Baibulo. Ndipo munkhani yachitatu, tidzakambirana zimene abale angachite kuti azigwiritsa ntchito moyenera udindo wawo mumpingo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena