Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: Apolisi amanga m’bale kunyumba kwake. Mkazi ndi mwana wake akuona pamene iwo akumutenga. Pamene m’baleyo ali kundende, abale ndi alongo abwera kunyumba kwake ndipo akuchita kulambira kwa pabanja ndi mkazi ndi mwana wake. Mayi ndi mwana wakeyo akumapemphera kwa Yehova pafupipafupi kuti awapatse mphamvu zotha kupirira mayesero amene akumana nawo. Yehova wawapatsa mtendere wamumtima ndipo wawathandiza kukhala olimba mtima. Zotsatira zake n’zakuti chikhulupiriro chawo chalimba kwambiri, zomwe zawathandiza kuti azipirira mosangalala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena