Mawu a M'munsi
a Munkhani yapitayi, tinakambirana zifukwa 4 zimene zinachititsa anthu ena m’mbuyomu kukana Yesu komanso zomwe zimachititsa anthu kukana kumvetsera otsatira ake masiku ano. Munkhaniyi tikambirana zifukwa zinanso 4. Tionanso chifukwa chake anthu oona mtima amene amakonda Yehova, salola kuti chilichonse chiwakhumudwitse n’kusiya kumutumikira.