Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zinthu zonse zabwino zimachokera kwa Yehova. Iye amapereka zinthu zabwino kwa aliyense, ngakhalenso kwa anthu oipa. Koma iye amakonda kuchitira zinthu zabwino makamaka atumiki ake okhulupirika. Munkhaniyi, tiona mmene Yehova amaperekera zinthu zabwino kwa atumiki ake. Tionanso njira yapadera yosonyeza mmene Yehova amaperekera zinthu zabwino kwa atumiki ake amene amasankha kuchita zambiri pomutumikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena