Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yehova ndi mnzathu wapamtima. Timaona kuti ubwenzi wathu ndi iye ndi wamtengo wapatali ndipo timafunitsitsa kuti timudziwe bwino. Pamatenga nthawi yaitali kuti tidziwane bwino ndi winawake. Choncho pangafunike nthawi yokwanira kuti tipitirize kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova. Popeza kuti masiku ano timakhala otanganidwa kwambiri, kodi tingatani kuti tizipeza nthawi yolimbitsa ubwenzi wathu ndi Atate wathu wakumwamba? Nanga kuchita zimenezi kungatithandize bwanji?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena