Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Amuna, akazi komanso ana ambirimbiri akulalikira mwakhama uthenga wabwino. Kodi inunso ndi m’modzi wa anthu amenewa? Ngati ndi choncho, dziwani kuti mukugwira nawo ntchito yomwe Ambuye wathu Yesu Khristu akutsogolera. Munkhaniyi, tiona umboni wosonyeza kuti Yesu akutsogolera ntchito yolalikirayi. Kuganizira zimenezi kutithandiza kuti tikhale otsimikiza kupitiriza kutumikira Yehova motsogoleredwa ndi Khristu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena