Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b TANTHAUZO LA MAWU ENA: “Paradaiso wauzimu” ndi mkhalidwe wotetezeka womwe timalambiriramo Yehova mogwirizana. Mumkhalidwe umenewu, tili ndi chakudya chambiri chauzimu chomwe si chosokonezedwa ndi mabodza a chipembedzo komanso tili ndi ntchito yabwino yolalikira uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu. Timakhala pa ubwenzi wabwino ndi Yehova ndipo timakhala mwamtendere ndi abale ndi alongo athu, omwe amatithandiza kupirira mosangalala mavuto omwe timakumana nawo. Timalowa m’paradaiso wauzimuyi tikayamba kulambira Yehova movomerezeka komanso tikamayesetsa kumutsanzira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena