Mawu a M'munsi
a Kodi nthawi zambiri mumaganizira mmene moyo udzakhalire m’Paradaiso? N’zolimbikitsatu kumachita zimenezi. Tikamaganizira kwambiri zimene Yehova adzatichitire m’tsogolo, m’pamenenso timaphunzitsa anthu ndi mtima wonse zokhudza dziko latsopano. Nkhaniyi itithandiza kuti tizikhulupirira kwambiri lonjezo la Yesu lokhudza Paradaiso.