Mawu a M'munsi
a Yehova akulonjeza kupereka mtendere kwa anthu amene amamukonda. Kodi mtendere umene Mulungu amaperekawo ndi chiyani, nanga tingaupeze bwanji? Kodi “mtendere wa Mulungu” ungatithandize bwanji ngati kwagwa miliri, kwachitika ngozi zam’chilengedwe kapenanso tikamazunzidwa? Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa.