Mawu a M'munsi
a Nthawi zambiri Yehova amagwiritsa ntchito atumiki ake okhulupirika pothandiza amene akukumana ndi mavuto. Angagwiritsenso ntchito inuyo polimbikitsa abale ndi alongo anu. Tiyeni tione mmene tingathandizire ena akakhala pa mavuto.
a Nthawi zambiri Yehova amagwiritsa ntchito atumiki ake okhulupirika pothandiza amene akukumana ndi mavuto. Angagwiritsenso ntchito inuyo polimbikitsa abale ndi alongo anu. Tiyeni tione mmene tingathandizire ena akakhala pa mavuto.