Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Atumiki onse a Yehova amayesetsa kuwerenga Mawu ake tsiku lililonse. Anthu enanso ambiri amawerenga Baibulo koma samvetsa zimene amawerengazo. Ndi mmenenso zinalili ndi anthu ena mu nthawi ya Yesu. Kuona zimene Yesu anauza anthu amene amawerenga Mawu a Mulungu, kungatithandize kuphunzira zinthu zina zomwe zingatithandize kuti tizipindula kwambiri tikamawerenga Baibulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena