Mawu a M'munsi
e Onaninso lemba la Mateyu 19:4-6 pomwe Yesu anafunsa Afarisi funso lomweli lakuti: “Kodi simunawerenge?” Ngakhale kuti iwo anali atawerenga nkhani yokhudza mmene Yehova analengera zinthu, ankanyalanyaza zomwe imaphunzitsa pankhani ya mmene Mulungu amaonera ukwati.