Mawu a M'munsi
f Lipoti lina linanena kuti patapita zaka zingapo, rabi wina ananena kuti: “M’dzikoli muli anthu osapitirira 30 olungama ngati mmene analili Abulahamu. Ngatidi alipo 30, ine ndi mwana wanga tili m’gulu limenelo, ngati alipo 10, ine ndi mwana wanga tili m’gulu limenelo, ngati alipo 5, ine ndi mwana wanga tili m’gulu limenelo, ngati alipo awiri, ndiye kuti ndi ine ndi mwana wanga, koma ngati alipo mmodzi, ndi ineyo.”