Mawu a M'munsi
a Timafuna kuti mapemphero athu azikhala ngati makalata osangalatsa, omwe talembera mnzathu wapamtima. Komabe si nthawi zonse pamene zimakhala zophweka kupeza nthawi yoti tipemphere. Ndiponso nthawi zina zingativute kudziwa nkhani zoti titchule m’mapemphero athu. Munkhaniyi tikambirana mfundo zofunika zimenezi.