Mawu a M'munsi
a Yehova amatitsimikizira kuti adzayankha mapemphero athu ngati ali ogwirizana ndi chifuniro chake. Pamene tikukumana ndi mayesero, sitingakayikire kuti adzatithandiza kukhalabe okhulupirika kwa iye. Tiyeni tione mmene Yehova amayankhira mapemphero athu.