Mawu a M'munsi
a Nthawi zambiri timalimbikitsidwa kuti tizidziikira zolinga zauzimu. Koma bwanji ngati tinadziikira kale cholinga china chomwe tikuvutika kuchikwaniritsa? Nkhaniyi ifotokoza zinthu zina zomwe zingatithandize kuti tikwaniritse zolinga zathu.