Mawu a M'munsi
b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Cholinga chauzimu ndi chilichonse chomwe mungayesetse kuti muzichichita bwino kapena kuchikwaniritsa n’cholinga choti muzitumikira Yehova mokwanira ndiponso muzimusangalatsa. Mwachitsanzo, mukhoza kukhala ndi cholinga chofuna kukulitsa khalidwe linalake, kapena kuti muzichita bwino pambali inayake yokhudza kulambira monga kuwerenga Baibulo, kuphunzira panokha kapena kulalikira.