Mawu a M'munsi
a Kungoyambira nthawi ya Adamu ndi Hava, Satana wakhala akulimbikitsa mfundo yakuti anthu azisankha okha chimene chili chabwino kapena choipa. Amafunanso kuti tiziwaona choncho malamulo a Yehova komanso malangizo amene gulu lake limatipatsa. Nkhaniyi itithandiza kuti tizipewa kukhala ndi maganizo odzidalira amene dziko lolamuliridwa ndi Satanali limalimbikitsa komanso kukhala otsimikiza kuti tizimvera Yehova.