Mawu a M'munsi
a Nkhaniyi ithandiza anthu amene akukumana ndi mavuto aakulu kapenanso amene apatsidwa utumiki umene akuona kuti sangaukwanitse. Tionanso mmene Yehova angatithandizire komanso zimene tingachite kuti atithandize.
a Nkhaniyi ithandiza anthu amene akukumana ndi mavuto aakulu kapenanso amene apatsidwa utumiki umene akuona kuti sangaukwanitse. Tionanso mmene Yehova angatithandizire komanso zimene tingachite kuti atithandize.