Mawu a M'munsi
a Bungwe lina loona za umoyo ku United States, linanena kuti kumwa mowa kwambiri kumabweretsa mavuto monga kupha anthu, kudzipha, nkhanza zokhudza kugonana, kuzunza mwamuna kapena mkazi wako, khalidwe lotayirira pa nkhani ya kugonana komanso kupita padera.