Mawu a M'munsi
a Mungapeze nkhani zolimbitsa chikhulupiriro pa jw.org polemba pamalo ofufuzira mawu akuti “tsanzirani chikhulupiriro chawo” kapena “zochitika pa moyo wa a Mboni za Yehova”. Pa JW Library, pitani pagawo lakuti Article Series kenako pamene alemba kuti “Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo” kapena “Mbiri ya Mboni za Yehova Zosiyanasiyana.”