Mawu a M'munsi
b Kuti mumve zambiri pa mawu akuti “chiwiya chosachedwa kusweka,” onani nkhani yakuti “Mtengo wa ‘Chotengera Chochepa Mphamvu’” mu Nsanja ya Olonda ya May 15, 2006, komanso yakuti “Malangizo Anzeru kwa Okwatirana” mu Nsanja ya Olonda ya March 1, 2005.