Mawu a M'munsi
a Ngakhale kuti m’Malemba a Chiheberi mawu akuti “wolimba” kapena “wosalimba” sapezekamo, mfundo yake imapezekamo. Mwachitsanzo, buku la Miyambo limasiyanitsa munthu yemwe ndi wamng’ono ndiponso wosadziwa zinthu ndi munthu wanzeru yemwe ndi womvetsa zinthu.—Miy. 1:4, 5.