Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Mfumu Asa anachita machimo aakulu. (2 Mbiri 16:​7, 10) Koma Baibulo limasonyeza kuti Yehova ankamuona kuti anachita zabwino. Ngakhale kuti poyamba anakana atadzudzulidwa, n’kutheka kuti pambuyo pake analapa. Koma zabwino zimene anachita ndi zambiri tikayerekezera ndi zimene analakwitsa. Chofunika kwambiri ndi chakuti Asa ankalambira Yehova yekha ndipo anayesetsa kuchotsa mafano mu ufumu wake.—1 Maf. 15:​11-13; 2 Mbiri 14:​2-5.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena