Mawu a M'munsi
c Kuti ‘tikhalenso pa ubwenzi wabwino’ ndi Yehova, tiyenera kusonyeza kuti talapa pomupempha kuti atikhululukire ndiponso kusintha khalidwe lathu. Ngati tachita tchimo lalikulu, tiyeneranso kupempha akulu kuti atithandize.—Yak. 5:14, 15.