Mawu a M'munsi
a MATANTHAUZO A MAWU ENA: Munkhaniyi tikukambirana za kukayikira ngati Yehova amatikonda kapenanso ngati tinasankha bwino. Sitikukambirana za kukayikira kumene Baibulo limasonyeza kuti ndi umboni wakuti sitikukhulupirira Yehova kapena malonjezo ake.