Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Aisiraeli ambiri omwe anaona zodabwitsa zimene Yehova anachita pa Nyanja Yofiira, sanakalowe m’Dziko Lolonjezedwa. (Num. 14:22, 23) Yehova analamula kuti anthu a zaka 20 kapena kuposa pamenepo adzafera m’chipululu. (Num. 14:29) Koma Yoswa, Kalebe, anthu ambiri a fuko la Levi ndi ena onse amene anali asanakwanitse zaka 20 anakhalabe ndi moyo ndipo anaona Yehova akukwaniritsa lonjezo lake pamene Aisiraeli anawoloka mtsinje wa Yorodano n’kukalowa m’dziko la Kanani.​—Deut. 1:24-40.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena