Mawu a M'munsi
a Kuti mudziwe zimene “kuganiza bwino” kumatanthauza, onani pa jw.org kapena pa JW Library, nkhani yakuti, “2 Timoteyo 1:7—Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha” pa gawo lakuti “Kufotokoza Mavesi a m’Baibulo,” pansi pa kamutu kakuti “Kuganiza bwino.”