Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pa nthawiyi, M’bale Peter Vanderhaegen ndi M’bale Len Davis, omwe anachita umishonale kwa zaka zambiri m’dzikoli, anali atapitirira zaka 60, moti dziko la Indonesia silinkawaonanso ngati amishonale. Komanso Mlongo Marian Tambunan (yemwe poyamba anali Marian Stoove) anali atakwatiwa ndi mwamuna wa ku Indonesia konko. Choncho anthu atatu onsewa analoledwa kukhalabe m’dzikoli. Onse anakhalabe okhulupirika ndipo ngakhale kuti ntchito yolalikira inali yoletsedwa, anthuwa sanasiye kulalikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena