Mawu a M'munsi
b Mungathenso kufufuza pa jw.org polemba mawu ofanana ndi zomwe mukufuna kusankhazo. Pawebusaitiyi pamapezeka malangizo a m’Malemba pa nkhani zosiyanasiyana. Kuwonjezera pamenepa, mungathenso kufufuza mu “Kalozera wa Mawu a m’Baibulo” mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika.