Mawu a M'munsi
c Maufulu ngati amenewa akupezekanso mu African Charter on Human and Peoples’ Rights, American Declaration of the Rights and Duties of Man, 2004 Arab Charter on Human Rights, Association of Southeast Asian Nations ndi mu Pangano la Dziko Lonse la Ufulu wa Anthu ndi wa Zandale. Komabe mayiko amene anavomereza mapangano amenewa amachita zosiyanasiyana potsatira maufulu amenewa.