Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Buku Lothandiza pa Moyo Wamakono
    Buku la Anthu Onse
    • Kusiyana ndi zimenezo, Baibulo limapereka uphungu wodalirika ndi wabwino pankhani ya ukwati. Limavomereza kuti nthaŵi zina zinthu zikafika poipa chisudzulo chimaloleka. (Mateyu 19:9) Komanso, limatsutsa kusudzulana pazifukwa zopanda kumutu. (Malaki 2:​14-16) Limatsutsanso kusakhulupirika mu ukwati. (Ahebri 13:4) Limatero kuti ukwati nkudzipereka: ‘Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.’a​—Genesis 2:​24; Mateyu 19:​5, 6.

  • Buku Lothandiza pa Moyo Wamakono
    Buku la Anthu Onse
    • a Liwu lachihebri lakuti da·vaqʹ, lotembenuzidwa kuti “nadzadziphatika” panopo, “lili ndi tanthauzo la kummamatira wina wake mwachikondi ndi mokhulupirika.”4 M’Chigiriki, liwu lotembenuzidwa kuti “nadzaphatikizana” pa Mateyu 19:5 lili paubale ndi liwu lotanthauza “kumamatiza,” “kuphatika ndi sementi,” “kulumikizana zolimba.”5

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena