Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Dzikoli Lidzatha Bwanji?
    Nsanja ya Olonda—2012 | September 15
    • 15. Kodi n’chiyani chidzachitikire Satana ndi ziwanda zake Aramagedo ikadzatha?

      15 Choyamba, Satana adzaona dziko lakeli likuwonongedwa mpaka kutheratu. Kenako idzafika nthawi yoti nayenso aone zokhoma. Mtumwi Yohane anafotokoza zimene zidzachitike. (Werengani Chivumbulutso 20:1-3.) Yesu Khristu, yemwe ndi “mngelo” wokhala ndi “kiyi wa paphompho,” adzagwira Satana ndi ziwanda zake n’kuwaponya m’phompho kuti akhale m’menemo zaka 1,000. (Luka 8:30, 31; 1 Yoh. 3:8) Ichi chidzakhala chiyambi cha kuphwanya mutu wa njoka.d—Gen. 3:15.

  • Kodi Dzikoli Lidzatha Bwanji?
    Nsanja ya Olonda—2012 | September 15
    • d Adzamalizitsa kuphwanya mutu wa njoka zikadzatha zaka 1,000 zimenezi. Pa nthawiyi, Satana ndi ziwanda zake adzaponyedwa “m’nyanja yamoto ndi sulufule.”—Chiv. 20:7-10; Mat. 25:41.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena