Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Moyo wa Makolo Akale
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • Panthaŵi ina m’tsogolo Yakobo (Israyeli) mwana wawo, anayenda ulendo wofananawo kuti akakwatire mkazi wolambira Yehova. Koma pobwerera kwawo, Yakobo anadutsa njira ina. Atawoloka Yaboki pafupi ndi Penieli, Yakobo analimbana ndi mngelo. (Gen. 31:21-25; 32:2, 22-30) Esau anakumana naye m’dera limenelo, ndipo Yakobo ndi Esau anakakhala kumadera osiyana.—Gen. 33:1, 15-20.

  • Moyo wa Makolo Akale
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • [Mitsinje]

      Yaboki

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena